2 Mafumu 1:3 BL92

3 Koma mthenga wa Yehova anati kwa Eliya wa ku Tisibe, Nyamuka, kwera kukomana ndi mithenga ya mfumu ya Samariya, nunene nayo, Kodi ndi popeza palibe Mulungu mwa Israyeli, kuti mukafunsira kwa Baala Zebubu mulungu wa ku Ekroni?

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 1

Onani 2 Mafumu 1:3 nkhani