13 Yehu anakomana nao abale a Ahaziya mfumu ya Yuda, nati, Ndinu ayani? Nati iwo, Ife ndife abale a Ahaziya, tirikutsika kulankhulira ana a mfumu, ndi ana a nyumba yaikuru.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10
Onani 2 Mafumu 10:13 nkhani