2 Mafumu 10:9 BL92

9 Ndipo kunali m'ma wa, iye anaturuka, naima, nati kwa anthu onse, Muli olungama inu, taonani, ndinapandukira mbuye wanga ndi kumupha; koma awa onse anawakantha ndani?

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 10

Onani 2 Mafumu 10:9 nkhani