14 Natenga golidi ndi siliva yense, ndi zotengera zonse anazipeza m'nyumba ya Yehova, ndi ku cuma ca m'nyumba ya mfumu, acikole omwe; nabwera kumka ku Samariya,
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 14
Onani 2 Mafumu 14:14 nkhani