2 Mafumu 14:27 BL92

27 Ndipo Yehova sadanena kuti adzafafaniza dzina la Israyeli pansi pa thambo; koma anawapulumutsa ndi dzanja la Yerobiamu mwana wa Yoasi.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 14

Onani 2 Mafumu 14:27 nkhani