2 Mafumu 15:20 BL92

20 Ndipo Menahemu anasonkhetsa Israyeli ndaramazi, nasonkhetsa acuma, yense masekeli makumi asanu a siliva: kuti azipereke kwa mfumu ya Asuri. Nabwerera mfumu ya Asuri osakhala m'dzikomo.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:20 nkhani