2 Mafumu 15:19 BL92

19 Pamenepo Puli mfumu ya Asuri anadza kudzamenyana ndi dziko, koma Menahemu anampatsa Puli matalente a siliva cikwi cimodzi; kuti dzanja lace likhale naye kukhazikitsa ufumu m'dzanja lace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:19 nkhani