2 Mafumu 15:5 BL92

5 Ndipo Yehova anadwaza mfumu, nakhala iye wakhate mpaka tsiku la imfa yace, nakhala m'nyumba ya padera. Ndipo Yotamu mwana wa mfumu anayang'anira banja la mfumu, naweruza anthu a m'dziko.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 15

Onani 2 Mafumu 15:5 nkhani