23 mpaka Yehova adacotsa Israyeli pamaso pace, monga adanena mwa dzanja la atumiki ace onse aneneriwo. Momwemo Israyeli anacotsedwa m'dziko lao kumka nao ku Asuri mpaka lero lino.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 17
Onani 2 Mafumu 17:23 nkhani