2 Mafumu 17:24 BL92

24 Ndipo mfumu ya Asuri anabwera nao anthu ocokera ku Babulo, ndi ku Kuta, ndi ku Ava, ndi ku Hamati, ndi ku Safaravaimu, nawakhalitsa m'midzi ya Samariya, m'malo mwa ana a Israyeli; nakhala iwo eni ace a Samariya, nakhala m'midzi mwace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 17

Onani 2 Mafumu 17:24 nkhani