2 Mafumu 19:21 BL92

21 Mau a Yehova akumnenera iye ndi awa, Namwali mwana wamkazi wa Ziyoni akunyoza, akuseka mwana wamkazi wa Yerusalemu, akupukusira mutu pambuyo pako.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 19

Onani 2 Mafumu 19:21 nkhani