1 Masiku ajawo Hezekiya anadwala, nafuna kufa. Namdzera Yesaya mneneri mwana wa Amozi, nanena naye, Atero Yehova, Siyira banja lako; pakuti udzafa, sudzakhala ndi moyo.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 20
Onani 2 Mafumu 20:1 nkhani