8 Nati Hezekiya kwa Yesaya, Cizindikilo cace nciani kuti Yehova adzandiciza, ndi kuti ndidzakwera kumka ku nyumba ya Yehova tsiku lacitatu?
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 20
Onani 2 Mafumu 20:8 nkhani