1 Manase anali wa zaka khumi ndi ziwiri polowa iye ufumu wace, nakhala mfumu zaka makumi asanu ndi zisanu m'Yerusalemu; ndi dzina la mace ndiye Hefisiba.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 21
Onani 2 Mafumu 21:1 nkhani