2 Mafumu 22:8 BL92

8 Ndipo Hilikiya mkulu wa ansembe anati kwa Safani mlembi, Ndapeza buku la cilamulo m'nyumba ya Yehova. Napereka Hilikiya bukulo kwa Safani, iye naliwerenga.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 22

Onani 2 Mafumu 22:8 nkhani