11 Nacotsanso akavalo amene mafumu a Yuda adapereka kwa dzuwa, polowera nyumba ya Yehova, ku cipinda ca Natani Meleki mdindoyo, cokhala kukhonde; natentha magareta a dzuwa ndi moto.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 23
Onani 2 Mafumu 23:11 nkhani