2 Mafumu 3:11 BL92

11 Koma Yehosafati anati, Palibe pano mneneri wa Yehova kodi, kuti tifunsire Yehova mwa iye? Ndipo wina wa anyamata a mfumu ya Israyeli anayankha, nati, Elisa mwana wa Safati ali pano, ndiye uja anathira madzi m'manja a Eliya.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 3

Onani 2 Mafumu 3:11 nkhani