17 Ndipo Namani anati, Mukakana, andipatse akatundu a dothi osenza nyuru ziwiri; pakuti mnyamata wanu sadzaperekanso nsembe yopsereza kapena yophera kwa milungu yina, koma kwa Yehova.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 5
Onani 2 Mafumu 5:17 nkhani