23 Ndipo anwakonzera cakudya cambiri, nadya namwa iwo; nawauza amuke; namuka kwa mbuye wao. Ndipo magulu a Aramu sanadzanso ku dziko la Israyeli.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6
Onani 2 Mafumu 6:23 nkhani