2 Mafumu 6:29 BL92

29 Ndipo tinaphika mwana wanga ndi kumudya, ndi mawa wace ndinanena naye, Tenga mwana wako, timudye; koma wambisa mwana wace.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6

Onani 2 Mafumu 6:29 nkhani