2 Mafumu 6:33 BL92

33 Akali cilankhulire nao, tapenyani, wamtsikira mthengayo; ndi mfumu inati, Taonani, coipa ici cicokera kwa Yehova; ndilindiranjinso Yehova?

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 6

Onani 2 Mafumu 6:33 nkhani