2 Mafumu 7:7 BL92

7 Nanyamuka, nathawa kuli sisiro, nasiya mahema ao, ndi akavalo ao, ndi aburu ao, misasa iri cimangire; nathawa, apulumutse moyo wao.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 7

Onani 2 Mafumu 7:7 nkhani