8 Ndipo pofika akhate ao polekezera pa misasa, analowa m'hema mmodzi, nadya namwa, natengako siliva ndi golidi ndi zobvala, namuka, nazibisa; nabwerera, nalowa m'hema mwina, natengako, namuka, nazibisa.
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 7
Onani 2 Mafumu 7:8 nkhani