14 Motero Yehu mwana wa Yehosafati mwana wa Nimsi anapandukira Yoramu. Tsono Yoramu atalindira ku Ramoti Gileadi, iye ndi Aisrayeli onse, cifukwa ca Hazaeli mfumu ya Aramu;
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9
Onani 2 Mafumu 9:14 nkhani