2 Mafumu 9:18 BL92

18 Ndipo anamuka wapakavalo kukomana naye, nati, Atero mfumu, Mtendere kodi? Nati Yehu, Ngwanji mtendere, tembenukira m'mbuyo mwanga. Ndi mlonda anawafotokozera kuti, Mthenga wawafika, koma wosabwera.

Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9

Onani 2 Mafumu 9:18 nkhani