36 Nabwerera iwo, namfotokozera. Nati iye, Ndiwo mau a Yehova ananena wo mwa mtumiki wace Eliya wa ku Tisibe, ndi koti, Pa munda wa Yezreeli agaru adzadya mnofu wa Yezebeli;
Werengani mutu wathunthu 2 Mafumu 9
Onani 2 Mafumu 9:36 nkhani