25 Monga kabvumvulu angopita, momwemo woipa kuti zi;Koma olungama ndiwo maziko osatha.
26 Ngati vinyo wowawa m'mano, ndi utsi m'maso,Momwemo wolesi kwa iwo amene amtuma.
27 Kuopa Yehova kutanimphitsa masiku;Koma zaka za oipa zidzafinimpha,
28 Ciyembekezo ca olungama ndico cimwemwe;Koma cidikiro ca oipa cidzaonongeka.
29 Njira ya Yehova ndi linga kwa woongoka mtima;Koma akucita zoipa adzaonongeka.
30 Wolungama sadzacotsedwa konse:Koma oipa sadzakhalabe m'dziko.
31 M'kamwa mwa wolungama mulankhula nzeru;Koma lilime lokhota lidzadulidwa.