30 Kuunika kwa maso kukondweretsa mtima;Ndipo pomveka zabwino mafupa amatenga uwisi.
31 Khutu lomvera cidzudzulo ca moyoLidzakhalabe mwa anzeru.
32 Wokana mwambo apeputsa moyo wace;Koma wosamalira cidzudzulo amatenga nzeru.
33 Kuopa Yehova ndiko mwambo wanzeru;Ndipo cifatso citsogolera ulemu.