1 Usacitire nsanje anthu oipa, Ngakhale kufuna kukhala nao;
2 Pakuti mtima wao ulingalira za cionongeko;Milomo yao ilankhula za mphulupulu.
3 Nzeru imangitsa nyumba;Luntha liikhazikitsa.
4 Kudziwa kudzaza zipinda zaceNdi cuma conse cofunika ca mtengo wace.