16 Wolesi adziyesa wanzeruKoposa anthu asanu ndi awiri akuyankha mozindikira.
17 Wakungopita ndi kubvutika ndi ndeu yosakhala yaceAkunga wogwira makutu a garu.
18 Monga woyaruka woponya nsakali,Mibvi, ndi imfa,
19 Momwemo wonyenga mnzace ndi kuti, Ndi kusewera kumeneku.
20 Posowa nkhuni moto ungozima;Ndi popanda kazitape makangano angoleka.
21 Monga makala ozizira pa makala akunyeka, ndi nkhuni pamoto;Momwemo munthu wamakangano autsa ndeu.
22 Mau a kazitape ndi zakudya zolongosokaZitsikira m'kati mwa mimba.