Luka 1:20 BL92

20 Ndipo taona, udzakhala wotonthola ndi wosakhoza kulankhula, kufikira tsiku limene zidzacitika izi, popeza kuti sunakhulupirira mau, anga, amene adzakwanitsidwa pa nyengo yace.

Werengani mutu wathunthu Luka 1

Onani Luka 1:20 nkhani