Luka 1:5 BL92

5 Masiku a Herode, mfumu ya Yudeya, kunali munthu wansembe, dzina lace Zakariya, wa gulu la ansembe la Abiya; ndi mkazi wace wa ana akazi a pfuko la Aroni, dzina lace Elisabeti.

Werengani mutu wathunthu Luka 1

Onani Luka 1:5 nkhani