Luka 11:26 BL92

26 Pomwepo, upita nutenga mizimu yina isanu ndi iwiri yoipa yoposa ndi uwu mwini; ndipo ilowa nikhalira komweko; ndipo makhalidwe otsiriza a munthu uyu aipa koposa oyambawo.

Werengani mutu wathunthu Luka 11

Onani Luka 11:26 nkhani