Luka 11:39 BL92

39 Koma Ambuye anati kwa iye, Tsopano inu Afarisi muyeretsa kunja kwace kwa cikho ndi mbale, koma m'kati mwanu mudzala zolanda ndi zoipa.

Werengani mutu wathunthu Luka 11

Onani Luka 11:39 nkhani