Luka 12:11 BL92

11 Ndipo pamene pali ponse adzamuka nanu ku mlandu wa m'sunagoge ndi kwa akulu, ndi aulamuliro, musade nkhawa ndi kuti mukadzikanira bwanji, ndipo ndi mau otani, kapena mukanena ciani;

Werengani mutu wathunthu Luka 12

Onani Luka 12:11 nkhani