Luka 12:24 BL92

24 Lingirirani makungubwi, kuti samafesai, kapena kutemai; alibe nyumba yosungiramo, kapena nkhokwe; ndipo Mulungu awadyetsa: nanga inu simuziposa mbalame kwambiri!

Werengani mutu wathunthu Luka 12

Onani Luka 12:24 nkhani