Luka 12:37 BL92

37 Odala akapolowo amene mbuye wao, pakudza iye, adzawapeza odikira; indetu ndinena ndinu, kuti iye adzadzimangira m'cuuno, nadzawakhalitsa pansi kudya, nadzafika, nadzawatumikira.

Werengani mutu wathunthu Luka 12

Onani Luka 12:37 nkhani