Luka 16:1 BL92

1 Ndipo iye ananenanso kwa ophunzira ace, Panali munthu mwini cuma, anali ndi kapitao wace; ndipo ameneyu ananenezedwa kwa iye kuti alikumwaza cuma cace.

Werengani mutu wathunthu Luka 16

Onani Luka 16:1 nkhani