Luka 16:15 BL92

15 Ndipo anati kwa iwo, Inu ndinu odziyesera nokha olungama pamaso pa anthu; koma Mulungu azindikira mitima yanu; cifukwa ici cimene cikuzika mwa anthu ciri conyansa pamaso pa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Luka 16

Onani Luka 16:15 nkhani