Luka 16:25 BL92

25 Koma Abrahamu anati, Mwana, kumbukila kuti unalandira zokoma zako pakukhala m'moyo iwe, momwemonso Lazaro zoipa; ndipo tsopano iye asangalatsidwa pano, koma iwe uzunzidwadi.

Werengani mutu wathunthu Luka 16

Onani Luka 16:25 nkhani