Luka 16:7 BL92

7 Pomwepo anati kwa wina, Ndipo iwe uli nao mangawa otani? Ndipo uyu anati, Mitanga ya tirigu zana iye ananena naye, Tenga kalata wako nulembere makumi asanu ndi atatu.

Werengani mutu wathunthu Luka 16

Onani Luka 16:7 nkhani