Luka 18:11 BL92

11 Mfarisiyo anaimirira napemphera izi mwa yekha, Mulungu, ndikuyamikani kuti sindiri monga anthu onse ena, opambapamba, osalungama, acigololo, kapenanso monga wamsonkho uyu;

Werengani mutu wathunthu Luka 18

Onani Luka 18:11 nkhani