Luka 18:13 BL92

13 Koma wamsonkhoyo alikuima patali sanafuna kungakhale kukweza maso kumwamba, komatu anadziguguda pacifuwa pace nanena, Mulungu, mundicitire cifundo, ine wocimwa.

Werengani mutu wathunthu Luka 18

Onani Luka 18:13 nkhani