Luka 18:31 BL92

31 Ndipo anadzitengera khumi ndi awiriwo, nati kwa iwo, Taonani, tikwera kunkaku Yerusalemu, ndipo zidzakwaniritsidwa kwa Mwana wa munthu zonse zolembedwa ndi aneneri.

Werengani mutu wathunthu Luka 18

Onani Luka 18:31 nkhani