Luka 2:21 BL92

21 Ndipo pamene panakwanira masiku asanu ndi atatu akumdula iye, anamucha dzina lace Yesu, limene anachula mngeloyo asanalandiridwe iye m'mimba.

Werengani mutu wathunthu Luka 2

Onani Luka 2:21 nkhani