Luka 21:25 BL92

25 Ndipo kudzakhala zizindikilo pa dzuwa ndi mwezi ndi nyenyezi; ndi pa dziko lapansi cisauko ca mitundu ya anthu, alikuthedwa nzeru pa mkukumo wace wa nyanja ndi mafunde ace;

Werengani mutu wathunthu Luka 21

Onani Luka 21:25 nkhani