Luka 21:34 BL92

34 Koma mudziyang'anire nokha, kuti kapena mitima yanu ingalemetsedwe ndi madyaidya ndi kuledzera, ndi zosamalira za moyo uno, ndi kuti tsiku ilo lingafikire inu modzidzimutsa ngati msampha;

Werengani mutu wathunthu Luka 21

Onani Luka 21:34 nkhani