Luka 22:47 BL92

47 Pamene iye anali cilankhulire, taonani, khamu la anthu, ndipo iye wochedwa Yudase, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anawatsogolera; nayandikira Yesu kumpsompsona iye.

Werengani mutu wathunthu Luka 22

Onani Luka 22:47 nkhani