Luka 3:22 BL92

22 ndipo Mzimu Woyera anatsika ndi maonekedwe a thupi lace ngati nkhunda, nadza pa iye; ndipo munaturuka mau m'thambo, kuti, Iwe ndiwe Mwana wanga wokondedwa, mwa Iwe ndikondwera.

Werengani mutu wathunthu Luka 3

Onani Luka 3:22 nkhani