Luka 4:1 BL92

1 Ndipo Yesu, wodzala ndi Mzimu Woyera, anabwera kucokera ku Yordano, natsogozedwa ndi Mzimu kunka kucipululu kukayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anai.

Werengani mutu wathunthu Luka 4

Onani Luka 4:1 nkhani